Yeremiya 8:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kodi anakhala ndi manyazi pamene anacita zonyansa? iai, sanakhala ndi manyazi, sananyala; cifukwa cace adzagwa mwa iwo amene akugwa, nthawi ya kuyang'aniridwa kwao adzagwetsedwa, ati Yehova.

Yeremiya 8

Yeremiya 8:11-21