Yeremiya 7:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kodi mudzapha, ndi kuba, ndi kucita cigololo, ndi kulumbira zonama, ndi kupereka nsembe kwa Baala, ndi kutsata milungu yina imene simunaidziwa,

Yeremiya 7

Yeremiya 7:7-17