Yeremiya 7:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi kuleka kutsendereza mlendo, ndi wamasiye, ndi mkazi wamasiye, osakhetsa mwazi wosacimwa m'malo muno, osatsata milungu yina ndi kudziipitsa nayo;

Yeremiya 7

Yeremiya 7:1-14