Yeremiya 7:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ana atola nkhuni, atate akoleza moto, akazi akanyanga ufa, kuti aumbe mikate ya mfumu yaikazi ya kumwamba, athirire milungu yina nsembe yothira, kuti autse mkwiyo wanga.

Yeremiya 7

Yeremiya 7:13-23