Yeremiya 7:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano, cifukwa munacita nchito zonsezi, ati Yehova, ndipo ndinanena kwa inu, ndi kuuka mamawa ndi kunena, koma simunamva; ndipo ndinakuitanani inu, koma simunayankha;

Yeremiya 7

Yeremiya 7:3-22