Yeremiya 6:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Monga kasupe aturutsa madzi ace, camweco aturutsa zoipa zace; ciwawa ndi kufunkha zimveka m'kati mwace; pamaso panga masiku onse pali kulira ndi mabala.

Yeremiya 6

Yeremiya 6:1-15