Yeremiya 51:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wamtokoma mmodzi adzathamanga kukakomana ndi mnzace, ndi mthenga mmodzi kukomana ndi mnzace, kukauza mfumu ya ku Babulo kuti mudzi wace wagwidwa ponsepo;

Yeremiya 51

Yeremiya 51:27-32