Yeremiya 50:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Lalikirani mwa amitundu, falikitsani, kwezani mbendera; falikitsani, musabise; munene, Babulo wagwidwa, Beli wacitidwa manyazi, Merodake watyokatyoka, zosema zace zacitidwa manyazi, mafano ace atyokatyoka.

Yeremiya 50

Yeremiya 50:1-6