Yeremiya 5:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Thamangani inu kwina ndi kwina m'miseu ya Yerusalemu, taonanitu, dziwani, ndi kufunafuna m'mabwalo ace, kapena mukapeza munthu, kapena alipo wakucita zolungama, wakufuna coonadi; ndipo ndidzamkhululukira.

Yeremiya 5

Yeremiya 5:1-3