22. ndi pa Diboni, ndi pa Nebo, ndi pa Beti-Dibilataimu;
23. ndi pa Kiriataimu, ndi pa Beti-Gamuli, ndi pa Beti-Meoni;
24. ndi pa Kerioti, ndi pa Bozira, ndi pa midzi yonse ya dziko la Moabu, yakutari kapena yakufupi.
25. Nyanga ya Moabu yaduka, ndipo watyoka mkono wace, ati Yehova.