Yeremiya 48:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwe mwana wamkazi wokhala m'Diboni, utsike pa ulemerero wako, nukhale ndi ludzu; pakuti wakufunkha Moabu wakukwerera, iwe waononga malinga ako.

Yeremiya 48

Yeremiya 48:16-28