Yeremiya 44:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace mkwiyo wanga ndi ukali wanga unathiridwa, nuyaka m'midzi ya Yuda ndi m'miseu ya Yerusalemu; ndipo yapasudwa nikhala bwinja, monga lero lomwe.

Yeremiya 44

Yeremiya 44:2-14