Yeremiya 40:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Gedaliya mwana wa Ahikamu mwana wa Safani anawalumbirira iwo ndi anthu ao, kuti, Musaope kuwatumikira Akasidi; khalani m'dzikomu, mutumikire mfumu ya ku Babulo, ndipo kudzakukomerani.

Yeremiya 40

Yeremiya 40:1-16