Yeremiya 4:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mukumbutse mitundu ya anthu; taonani, lalikirani Yerusalemu, kuti owazinga ndi nkhondo afumira ku dziko lakutari, nainenera midzi ya Yuda mau ao.

Yeremiya 4

Yeremiya 4:6-26