Yeremiya 38:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mbuyanga mfumu, anthu awa anacita zoipa m'zonse anacitira Yeremiya mneneri, amene anamponya m'dzenje; ndipo afuna kufa m'menemo cifukwa ca njala; pakuti mulibe cakudya cina m'mudzimu.

Yeremiya 38

Yeremiya 38:6-14