Yeremiya 37:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Yehova, Mulungu wa Israyeli: Muzitero kwa mfumu ya Yuda, imene inakutumani inu kwa Ine kuti mundifunse Ine: Taonani, nkhondo ya Farao, yakuturukira kudzathandiza inu, idzabwerera ku Aigupto ku dziko lao.

Yeremiya 37

Yeremiya 37:1-16