Yeremiya 31:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti nditatembenuka, ndinalapa; nditalangizidwa, ndinamenya pa ncafu yanga; ndinakhala ndi manyazi, inde, ndinapepulidwa, cifukwa ndinasenza citonzo ca ubwana wanga.

Yeremiya 31

Yeremiya 31:12-21