Yeremiya 31:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo namwali adzasangalala m'masewero, ndi anyamata ndi nkhalamba pamodzi; pakuti ndidzasandutsa kulira kwao kukhale kukondwera, ndipo ndidzatonthoza mitima yao, ndi kuwasangalatsa iwo asiye cisoni cao.

Yeremiya 31

Yeremiya 31:9-15