Yeremiya 3:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Masiku omwewo nyumba ya Yuda idzayenderana ndi nyumba ya Israyeli, ndipo adzaturuka pamodzi ku dziko la kumpoto kunka ku dziko limene ndinapatsa makolo anu kuti alowemo.

Yeremiya 3

Yeremiya 3:16-23