Yeremiya 26:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panalinso munthu amene ananenera m'dzina la Yehova, Uriya mwana wace wa Semaya wa ku Kiriati Yearimu; ndipo iye ananenera mudzi uwu ndi dziko lino monga mwa mau lonse a Yeremiya;

Yeremiya 26

Yeremiya 26:16-24