Yeremiya 26:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo akuru ndi anthu onse anati kwa ansembe ndi kwa aneneri, Munthu uyu sayenera kufa: pakuti watinenera ife m'dzina la Yehova Mulungu wathu.

Yeremiya 26

Yeremiya 26:12-18