Yeremiya 26:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene akuru a Yuda anamva zimenezi, anakwera kuturuka ku nyumba ya mfumu kunka ku nyumba ya Yehova; ndipo anakhala pa khomo la cipata catsopano ca nyumba ya Yehova.

Yeremiya 26

Yeremiya 26:5-17