Yeremiya 25:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kuwani, inu abusa, lirani, gubudukani, inu akuru a zoweta; pakuti masiku a kuphedwa kwanu akwanira ndithu, ndipo ndidzakuphwanyani inu, ndipo mudzagwa ngati cotengera cofunika.

Yeremiya 25

Yeremiya 25:32-38