Yeremiya 23:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

amene aganizira kuti adzaiwalitsa anthu anga dzina langa, ndi maloto ao amene anena munthu yense kwa mnansi wace, monga makolo ao anaiwala dzina limene ndimcha nalo Baala.

Yeremiya 23

Yeremiya 23:18-34