Yeremiya 23:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace njira yao idzakhala kwa iwo yonga malo akuterereka m'mdima; adzacotsedwa, nadzagwa momwemo; pakuti ndidzawatengera zoipa, caka ca kulangidwa kwao, ati Yehova.

Yeremiya 23

Yeremiya 23:2-22