Yeremiya 20:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma, Inu Yehova wa makamu, amene muyesa olungama, amene muona imso ndi mtima, mundionetse ine kubwezera cilango kwanu pa iwo; pakuti kwa inu ndaululira mlandu wanga.

Yeremiya 20

Yeremiya 20:8-18