Yeremiya 2:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ansembe sanati, Ali kuti Yehova? ndi iwo amene agwira malamulo sandidziwa Ine; ndi abusa omwe anandilakwira Ine, ndi aneneri ananenera mwa Baala, natsata zinthu zosapindula.

Yeremiya 2

Yeremiya 2:2-11