Yeremiya 16:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace, taonani, masiku adza, ati Yehova, kuti sadzanenanso, Pali Yehova, amene anakweza ana a Israyeli kuwaturutsa m'dziko la Aigupto.

Yeremiya 16

Yeremiya 16:12-16