Yeremiya 15:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mau anu anapezeka, ndipo ndinawadya; mau anu anakhala kwa ine cikondwero ndi cisangalalo ca mtima wanga; pakuti ndachedwa dzina lanu, Yehova Mulungu wa makamu.

Yeremiya 15

Yeremiya 15:11-21