Yeremiya 12:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ngakhale abale ako, ndi nyumba ya atate wako, ngakhale iwo anakunyenga iwe; ngakhale anakupfuulira iwe; usamvere iwo, ngakhale anena nawe mau abwino.

Yeremiya 12

Yeremiya 12:1-14