Yeremiya 10:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mafanowa akunga mtengo wakanjedza, wosemasema, koma osalankhula; ayenera awanyamule, pakuti sangathe kuyenda. Musawaope; pakuti sangathe kucita coipa, mulibenso mwa iwo kucita cabwino.

Yeremiya 10

Yeremiya 10:1-7