Yeremiya 1:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndisanakulenge iwe m'mimba ndinakudziwa, ndipo usanabadwe ndinakupatula iwe; ndinakuika kuti ukhale mneneri wa mitundu ya anthu.

Yeremiya 1

Yeremiya 1:1-10