Yakobo 4:16-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Koma tsopano mudzitamandira m'kudzikuza kwanu; kudzitamandira kuli konse kotero nkoipa.

17. Potero kwa iye amene adziwa kucita bwino, ndipo sacita, kwa iye kuli cimo.

Yakobo 4