Yakobo 1:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mapembedzedwe oyera ndi osadetsa pamaso pa Mulungu ndi Atate ndiwo: z kuceza ndi ana amasiye ndi akazi amasiye m'cisautso cao, ndi 1 kudzisungira mwini wosacitidwa mawanga ndi dziko lapansi.

Yakobo 1

Yakobo 1:24-27