Tito 2:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Koma iwe, lankhula zimene ziyenera ciphunzitso colamitsa:

2. okalamba akhale odzisunga, olemekezeka, odziletsa, olama m'cikhulupiriro, m'cikondi, m'cipiriro.

3. Momwemonso akazi okalamba akhale nao makhalidwe oyenera anthu oyera, osadierekeza, osakodwa naco cikondi ca pavinyo, akuphunzitsa zokoma;

4. kuti akalangize akazi ang one akonde amuna ao, akonde ana ao,

Tito 2