Rute 4:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Boazi kwa akulu, ndi kwa anthu onse, Inu ndinu mboni lero lino kuti ndagula zonse za Elimeleki, ndi zonse za Kilioni, ndi Maloni, pa dzanja la Naomi.

Rute 4

Rute 4:1-14