Rute 4:17-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Ndi akazi anansi ace anamucha dzina, ndi kuti, Kwa Naomi kwambadwira mwana; namucha dzina lace Ohedi; ndiye atate wa Jese atate wa Davide.

18. Iyo ndiyo mibadwo ya Perezi; Perezi anabala Hezironi;

19. ndi Hezironi anabala Ramu, ndi Ramu anabala Aminadabu;

20. ndi Aminadabu anabala Nasoni, ndi Nasoni anabala Salimoni;

Rute 4