17. Ndi akazi anansi ace anamucha dzina, ndi kuti, Kwa Naomi kwambadwira mwana; namucha dzina lace Ohedi; ndiye atate wa Jese atate wa Davide.
18. Iyo ndiyo mibadwo ya Perezi; Perezi anabala Hezironi;
19. ndi Hezironi anabala Ramu, ndi Ramu anabala Aminadabu;
20. ndi Aminadabu anabala Nasoni, ndi Nasoni anabala Salimoni;