Rute 4:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nakhale uyu wakukubwezera moyo, ndi wodyetsa ukalamba wako; pakuti mpongozi wako amene akukonda, amene aposa ana amuna asanu ndi awiri kukuthandiza, anambala.

Rute 4

Rute 4:13-21