Oweruza 8:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Gideoni anawapanga fano, naliika m'mudzi mwace, ndiwo Ofira; ndi Israyeli yense analitsata kuligwadira pomwepo; ndipo linakhala kwa Gideoni ndi nyumba yace ngati msampha.

Oweruza 8

Oweruza 8:17-35