Oweruza 8:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati kwa Yeteri mwana wace woyamba, Tauka, nuwaphe. Koma mnyamatayo sanasolola lupanga lace; pakuti anaopa, pokhala anali mnyamata.

Oweruza 8

Oweruza 8:12-26