Oweruza 6:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa iye, Ha! Mbuye, ndidzapulumutsa Israyeli ndi ciani? Taonani, banja langa liri loluluka m'Manase, ndipo ine ndine wamng'ono m'nyumba ya atate wanga.

Oweruza 6

Oweruza 6:7-22