Oweruza 5:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Galamuka, Debora, galamuka,Galamuka, galamuka, unene nyimbo;Uka, Baraki, manga nsinga ndende zako, mwana wa Abinoamu, iwe.

Oweruza 5

Oweruza 5:5-21