Oweruza 2:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndiponso mbadwo uwu wonse unasonkhanidwa kuikidwa kwa makolo ao; nuuka mbadwo wina pambuyo pao; wosadziwa Yehova kapena nchitoyi adaicitira Israyeli,

Oweruza 2

Oweruza 2:1-18