Oweruza 16:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma wina anauza a ku Gala, ndi kuti, Samsoni walowa kuno. Pamenepo anamzinga, namlalira usiku wonse pa cipata ca mudzi, nakhala cete usiku wonse ndi kuti, Tidikire mpaka kuca, pamenepo tidzamupha,

Oweruza 16

Oweruza 16:1-4