Oweruza 13:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Manowa anapembedza Yehova, nati, Yehova, ndikupemphani, atidzerenso munthu wa Mulungu mudamtumayo, natilangize ico tizicitira mwanayo akadzabadwa.

Oweruza 13

Oweruza 13:2-11