Oweruza 13:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pakuti taona, udzaima, nudzabala mwana wamwamuna; pamutu pace sipadzafika lumo; pakuti mwanayo adzakhalira kwa Mulungu Mnaziri cibadwire; nadzayamba iye kupulumutsa Israyeli m'dzanja la Afilisti.

Oweruza 13

Oweruza 13:2-7