Oweruza 11:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nawakantha kuyambira ku Aroeri mpaka ufika ku Miniti, ndiyo midzi makumi awiri, ndi ku Abelikerami, makanthidwe akuru ndithu. Motero ana a Amoni anagonjetsedwa pamaso pa ana a Israyeli.

Oweruza 11

Oweruza 11:22-34