Oweruza 1:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ana a Benjamini sanaingitsa Ayebusi okhala m'Yerusalemu; koma Ayebusi anakhala m'Yerusalemu pamodzi ndi ana a Benjamini, mpaka lero lino.

Oweruza 1

Oweruza 1:18-23