Oweruza 1:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yuda anamuka kwa Akanani akukhala m'Hebroni; koma kale dzina la Hebroni ndilo mudzi wa Ariba; ndipo anakantha Sesai, ndi Ahimani, ndi Talimai.

Oweruza 1

Oweruza 1:6-14