Obadiya 1:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akakudzera akuba, kapena mbala usiku, (Ha! waonongeka) sadzaba mpaka adzakhuta kodi? Akakudzera akuchera mphesa sadzasiya khunkha kodi?

Obadiya 1

Obadiya 1:4-15